Kuhyuka kwa Yesu
1 Chipano nifuna kukumbuchani anyiimwe abale wanga, ujha Uthenga Wabwino nidakulalikilani, namwenjho mudaikhulupilila, ni kuima nganganga. 2 Kupitila Uthenga Wabwino mulamichidwa, ikakhala ngati mupotela njhito Uthenga uwo nidakulalikilani, ila ngati simusiye, kukhulupilila kwanu kudali kwachajhe.