Chigololo chiwananga gulu lamkhulupilila Yesu
1 Navela kuti kwanu kuli chigololo, ni chigololo icho sichidakhalepo ata kwa wandhu yao siamjhiwa Mnungu, nakambilidwa pakati panu mmojhi wakhala ni wamkazi wa atate wake. 2 Namwe mujhidama, bwanji ata simudandaula, nikumchocha pakati panu mmeneyo wachita chigololo chimenecho.