11 Chipano, achabale, nikulailani! Mkhale okwanila, gwilani mayaluzo yanga, mkhale chindhu chimojhi, mkhale kwa mtendele. Mnungu wa chikondi ni mtendele siwakhale pamojhi namwe.
12 Pajha mpezana mlonjelane kwa chikondi cha chikondi.
13 Wandhu wonjhe a Mnungu kumeneko akulonjelani.
14 Nikufunilani ubwino wa Ambuye Yesu Kilisito ni chikondi cha Mnungu ni umojhi wa Mzimu wa Mnungu, vikhale namwe mwaonjhe.