Kulekelela wandhu wolakwa
5 Ikakhala pali mundhu walakwa, siwadanilakwile inepe, nambho wakulakwilani mwaonjhe. Nikamba chimwechi dala nisakhala okalipa kupunda. 6 Chilango icho wadachipata kuchokela kwa ambili wanu chamkwana. 7 Icho chakhalila kwanu, mbasa kumlekelela mundhu mmeneyo ni mkumthila mtima, siwadakhala ni chisoni kupunda ni kufelatu mtima. 8 Chimwecho nikupembhani kupunda mchimikizileninjho chikondi mundhu uyo walakwa.