Poolo waendela mujhi wa Kolinto
1 Pambuyo pa yameneyo, Poolo wadachoka ku mujhi wa Asene ni kupita kumujhi wa Kolinto. 2 Yapo wadali ku mujhi wa Kolinto wadakomana ni Muyahudi uyo wamatanidwa Akila, uyo wadabadwila mu mujhi wa Ponto, uyo wadali wangofika posachedwa kuchokela ku Italiya pamojhi ni mkazake, pakuti mchogoleli Kilaudia wadalamula Ayahudi onjhe achoke ku Loma. Poolo wadapita kwaayendela anyiiwo, 3 Poolo wadakhala kumweko ni kuchita njhito pamojhi ni anyiiwo, pakuti nayo wadali wokonja mahema ngati anyiiwo.