22 "Anyiiwme wandhu a ku Izilaeli vechelani mawu yaya niyakamba. Yesu wa ku Nazaleti wadali mundhu uyo wadachimikizidwa kwanu ni Mnungu kupitila vodabwicha, vozizicha ni vizindikilo, ivo Mnungu wadavichita pakati panu kupitila iye, ngati umo mwachinawene wake mujhiwila. 23 Kuyambila mmayambo Mundhu wadafuna anyiimwe mumphe Yesu, ni anyiimwe mdampha kwa kwasiila wandhu woipa ampachike pamtanda. 24 Nambho Mnungu wadamhyukicha ni kumchocha kupweteka kwa nyifa. Pakuti siidakhozeke kuti mbhavu za nyifa zimmange iye ngati mundhu womangidwa mndende.