41 Wandhu ambili adakhulupilila mawu ya Petulo ni adabatizidwa, wandhu ngati elufu zitatu adawonjezekela pa gulu lawo siku limenelo. 42 Wonjhe adali kuvechela mayaluzo ya atumwi kila siku, amakomana pamojhi niadya chakudya cha Ambuye ni kupembhela.
Ukhalo wa wandhu wajha amkhulupilila Kilisito
43 Wandhu wonjhe adali pajha adali ni mandha ndande ya vodabwicha vambili ni vizindikilo ivo vidachitidwa ni atumwi. 44 Wokhulupilila wonjhe adali ni maganizo yamojhi, ni amachita kila kandhu kwa mgwilizano. 45 Adagulicha vyuma vawo ni vindhu ivo adalinavo, adamgawila kila mudhu kulingana ni umo wadafunila. 46 Masiku yonjhe amakomana mmakhumbi la Nyumba ya Mnungu kwa mtima umojhi. Amadya chakudya pamojhi mmanyumba zao kwa kukondwela ni kwa mtima woyela, 47 niamtamanda Mnungu ni wandhu wonjhe adaakonda atumwi ameneo, siku zonjhe Ambuye amachulucha wandhu yao amaomboledwa.