Pular para o conteúdo
Publicidade

Maluko 4

39 Ndiipo Yesu wadauka ni kuunyindila mwela, "Khala chete!" Pampajha mwela udasiya ni nyanja idagona.

40 Chimwecho Yesu wadaakambila oyaluzidwa wake, "Ndande yanji muopa? Bwanji, mkali mlibe chikulupililo?"

41 Oyaluzidwa wake adaopa kupunda, adafunjhana, "Mundhu wa mtundu wanji uyu mbaka mwela umvela?"

Veja também