Pular para o conteúdo
Publicidade

1 Coríntios 6

15 Mujhiwa kuti mathupi yanu ni viwalo va thupi la Kilisito. Mukhoza kutenga chiwalo cha thupi la Kilisito ni kuchichita malo ya thupi la hule? Siikhozeka! 16 Pakuti uyo walunjana ni hule wakhala thupi limojhi ni huleyo yalembedwa mmalembo ya Mnungu, "Nao awili akhala thupi limojhi." 17 Nambho iye walunjana ni Ambuye wakhala mzimu umojhi ni Ambuye.

Veja também