2 Bwanji simujhiwa kuti wandhu a Mnungu sialamule wandhu siamjhiwa Mnungu? Ikakhala wandhu yawo siamjhiwa Mnungu sialamulidwe ni anyiimwe, ndande yanji simudalamulila ata vindhu vaving’ono? 3 Bwanji mujhiwa kuti sitaalamule niatumiki a kumwamba a Mnungu? Bwanji yaya siyadapitilile umo tikhalila pajhiko!
Publicidade