8 Chipano nikukambilani anyiimwe simuda kwate, nimwafedwa ni achamunanu, mbasa muendekele kukhala popande kukwata ni kukwatiwa ngati umo nili ine. 9 Nambho ngati simukhoza kuchekeleza makhumbilo yanu, chimwecho mkwate kapina kukwatiwa, pakuti mbasa kukwata kapina kukwatiwa kusiyana nikuhla ni kukhumbila.
10 Nambho kwa anyiwajha akwata nili ni lamulo. Wamkazi siwadasiyana ni mmunake, 11 nambho ikakhala wamkazi wasiyana nimmunake, siwada kwatiwa, kapina wabwelelane ni mmunake, ni wammuna siwadalemba kalata ya kumsiya mkazake.