Pular para o conteúdo
Publicidade

2 Coríntios 1

Poolo wamuyamika Mnungu

3 Watamandidwe Mnungu ni Tate wa Mbuye wathu Yesu Kilisito, Tate uyo wali ni lisungu ni Mnungu watithila mtima. 4 Iye watithila mtima pa kulaga kwathu konjhe, dala nafe tathile mtima wina yawo alaga, pakwathila mtima ngati umo Mnungu watithilila ife mtima. 5 Ngati umo tipundila kupata mavuto ndande ya kumkhulupilila Kilisito, ni mtundu umweo nde umo tipundila kuthilidwa mtima. 6 Tikalaga nde kuti ndande ya kuthilidwa mtima ni uomboli wanu. Tikathilidwa mtima, ndande ya kukuthilani mtima anyiimwe ni kukuthangatilani kuti mpate mbhavu ya kulimbila mtima pa mavuto yamweyajha tivutika ife. 7 Chikhulupililo icho tilinacho ndande ya anyiimwe ni chachikulu, tijhiwa kuti ngati umo tigwilizana pa mavuto yathu, chinchijha sitigwilizane kuthilana mtima uko tikulandila kwa Mnungu.

Veja também