6 Poolo yapo wadajhiwa kuti wandhu wina mgulu mujha adali Asadukayo ni wina adali Afalisayo, wadakweza mvekelo wake niwakamba, "Abale wanga aku ayahudi! Ine ni Mfalisayo, mwana wa Mfalisayo. Napelekedwa pa bwalo la milandu ndande nikhulupilila kuti wandhu yawo amwalila siahyuke!"