4 Uyo wali ni chikondi waembekeza, wathangatila, uyo wali nichikondi walibe njhanje, walibe dama, kapina kujhiona, 5 uyo wali ni chikondi siwachepa ulemu, uyo wali ni chikondi siwafuna vindhu va kumthangatila mwene, kapina mbhwai za msanga, siwasunga chikumbukilo cha voipa, 6 mundhu wa chikondi siwakondwela voipa, nambho chikondwela uzene. 7 Mundhu wachikondi wapilila yonjhe, mundhu wa chikondi wakhulupila wina, mundhu wa chikondi waembekeza, ni siwalepela.
8 Chikondi chiendekela sikuzonjhe, nambho ukakhalapo ulosi siuthele, ikakhalapo mikambo siithela kukakhalapo kujhiwa nako sikuthele.