Pular para o conteúdo
Publicidade

1 Coríntios 6

9 Zene mujhiwa kuti anyiyawo achita voipa siapata ufumu wa Mnungu. Simdanyengeka Achigololo, kapina alambila viboliboli kapina akomana chithupi kumbuyo kwa maumbidwe, 10 kapina anghungu, kapina akhumbila kuipa, kapina alojhela, kapina otukwana, kapina alanda anyiyawa siaupata Ufumu wa Mnungu. 11 Akumojhi wanu adali amtundu umeneo. Nambho mudachukidwa ni mdakhala bwino kwa kuchochedwa machimo ni Mnungu, mwavomelezeka ni Mnungu kwa Ambuye Yesu Kilisito ni kwa Mzimu wa a Mnungu wathu.

Veja também