Yesu waoneka muulemelelo wake
2 Pambuyo pa masiku sita, Yesu wadaatenga Petulo ni Yakobo ni Yohana, wadapita nawo ku phili, kumalo kopande wandhu. Pamwepo Yesu wadang’anamuka nghope yake pamaso pawo,
2 Pambuyo pa masiku sita, Yesu wadaatenga Petulo ni Yakobo ni Yohana, wadapita nawo ku phili, kumalo kopande wandhu. Pamwepo Yesu wadang’anamuka nghope yake pamaso pawo,