Publicidade

1 Coríntios 6

15 Mujhiwa kuti mathupi yanu ni viwalo va thupi la Kilisito. Mukhoza kutenga chiwalo cha thupi la Kilisito ni kuchichita malo ya thupi la hule? Siikhozeka! 16 Pakuti uyo walunjana ni hule wakhala thupi limojhi ni huleyo yalembedwa mmalembo ya Mnungu, "Nao awili akhala thupi limojhi." 17 Nambho iye walunjana ni Ambuye wakhala mzimu umojhi ni Ambuye.

18 Chithaweni chigololo. Machimo yina yonjhe wachita mundhu wachita kubwalo kwa thupi lake, nambho mundhu uyo wachita chigololo wachita mkhati mwathupi lake mwene wake. 19 Simujhiwa kuti mathupi yanu ni nyumba ya Mzimu Wamnungu, uwo ukhala mkati mwanu ni uwo mwapachidwa ni Mnungu? Mathupi yanu osati yanu mwachinawene nambho ni ya Mnungu, 20 pakuti mdaghulidwa kwa mtengo wa ukulu. Tumilani matupi yanu kwa ulemelelo wa Mnungu.

Veja também

Bíblia Online Bíblia Online

Bíblia Online • Versão: 2026-07-05_19-25-13-