3 Yesu wadamuyangha, "Uzene nikukambila, mundhu ngati siwabadwa kakawili siwakhoza kuuona Ufumu wa Amnungu."
4 Ndiipo Nikodemo wadamfunjha, "Mzee wakhoza bwanji kubadwanjho? Siwakhoze bwanji kulowa mmimba mwa amaye wake nikubaadwanjho?"
5 Yesu wadayangha, "Uzene nikukambila, mundhu ngati siwabadwa kwa majhi ni Mzimu, siwakhoza kulowa mu Ufumu wa Amnungu 6 Mundhu wabadwa chithupi kwa atate wake ni amake, nambho wabadwa Chizimu kwa Mzimu woyela. 7 Siudadabwa pakuti nakukambila kuti lazima kubadwanjho. 8 Mbhepo iputa ni kupita uko ifuna, uvela mvekelo wake, nambho siujhiwa uko ichoka kapina uko ipita. Nde umo ili kwa mundhu uyo wabadwa kwa Mzimu woyela."