Maliya waimba kumkweza Mnungu
46 Maliya wadakamba,
"Mtima wanga umkweza Ambuye,
47 ni mtima wanga ukondwela ndande ya Mnungu Muomboli wanga.
48 Pakuti Mnungu wanikumbukila kwa lisungu ine mbowa wake wojhichicha. Kuyambila chipano mibadwa yonjhe siinitane wamwawi.
49 Pakuti Mnungu wambhavu zonjhe wanichitila vavikulu,
jhina lake ni woyela.