Ifunika kuchezelela
34 "Mchenjele, mitima yanu siidalemeledwa ni ludyo ni kulojhela ni kulaga ndande ya umoyo uno, dala siku lijha silidakuphezani anyiimwe mwachizulumukila. 35 Pakuti siku limenelo silaafikile wandhu wonjhe yao akhala pajhiko lonjhe lapanjhi. 36 Mchezelele ni kupemphela nyengo zonjhe kuti mpheze mbhavu za kupulumuka yonjhe yayo siyachokele, kuti mukhoze kuima pamaso pa Mwana wa Mundhu."