12 Ujhulo, atumwi khumi ni awili wajha adafika kwa Yesu ni kumkambila, "Alaileni wandhu yawa apite kumijhi ni kuminda ili pafupi uko akhoza kupata chakudya ni malo yogona, pakuti pano tili ni paphululu." 13 Nambho Yesu wadayangha, "Anyiimwe nde mwapache chakudya." Anyiiwo adayangha ni kumkambila, "Tili ni mabumunda yasano ni njhomba ziwilipe. Pina tipite tikaagulile chakudya chokwana wandhu wonjhewa?" 14 Wandhu yawo adali pajha, adali wachimuna ngati 5,000.
Ndiipo, Yesu wadakambila atumwi wake, "Akambileni wandhu akhale panjhi mmagulu ya wandhu amsiniamsini." 15 Atumwi khumi ni awili wajha adachita ngati umo adakambilidwa, nawonjho adakhazika wandhu wonjhe. 16 Ndiipo, Yesu wadatenga mabumunda yasano ni njhomba ziwili zijha, wadapenya kumwamba, wadamuyamika ni kumtamanda Mnungu, wadaibandhula mabumunda ni kwapacha wajha atumwi wake kuti wagawile wandhu. 17 Wandhu wonjhe adadya ni kukhuta. Ni atumwi adakusanya vibandhu ivo vidakhala, adavijhaza mu miseche yokwana khumi ni yawili.