61 Mundhu mwina wadamkambila Yesu, "Ambuye, sinikuchateni, nambho munilole uti nipite nikalaile wandhu a kukhom langa." 62 Yesu wadamkambila, "Palibe mundhu uyo wagwila khasu ni kuyamba kulima wapenyanjho mmbuyo, mundhu mmeneyo siwafunika kulowa mu Ufumu wa Mnungu."