Pular para o conteúdo
Publicidade

Mateus 19

23 Pamenepo Yesu wadaakambila oyaluzidwa wake, "Zene nikukambilani, siikhale kolimba kwa mundhu wopata kulowa mu Ufumu wa kumwamba. 24 Nikukambilaninjho, ikhozeka chinyama icho chitanidwa ngamila kupyola pa ndhoolo kasindano kusiyana ni mundhu wopata kulowa mu Ufumu wa Mnungu."

25 Oyaluza wake yapo adavela chimwecho adadabwa, adamfunjha, "Chipano ni yani uyo wakhoza kuomboledwa?"

26 Yesu wadaapenyecha ni wadakambila, "Vindhu ivi kwa mundhu sivikhozekana, nambho kwa Mnungu vindhu vonjhe vikhozeka."

Veja também