Publicidade

Mateus 8

Yesu wamlamicha mundhu wa makate

1 Yesu yapo wadachika kuphili, gulu la likulu la wandhu lidamchata. 2 Mundhu mmojhi uyo wadali ni makate wadamchata Yesu, wadamgwadila ni kukamba, "Ambuye, mkafuna, mkoza kunilamicha kuti nikhoze kumlambila Mnungu!"

3 Yesu wadatambasula jhanja lake, nikumgafya wodwalayo ni kumkambila, "Nifuna! Ulame." Pampajha mundhuyo wadalama makate yake. 4 Ndiipo Yesu wadamkambila, "Vechela, usadamkambila mundhu waliyonjhe, nambho pita ukajhilangize kwa ajhukulu, ni kuchocha njhembe iyo yalamulidwa ni Musa kuwachimikhizila wandhu wonjhe kuti walama."

Yesu wamlamicha mbowa wa mkulu wa loma

5 Yesu yapo wadalowa ku Kapelinaumu, wamkulu wa gulu la asilikali mmojhi wa kuloma, wadamchata ni wadampembha wamthangatile. 6 Ndiipo wadakamba, "Imwe Ambuye, mbowa wanga wagona kukhomo, wavuwala ni wadwala kupunda."

7 Yesu wadamkambila, "Sinijhe kumlamicha."

8 Nambho yujha wamkulu waloma wadamkambila, "Imwe Ambuye, ine sinifunika imwe mulowe mnyumba mwanga, nambho chochani lamulope, ni mbowa wanga siwalame. 9 Pakuti ata ine nichogozedwa ni waakuluakulu wina, nilinawo asikali yao naachogoza. Nimlamula mmojhi, ‘Pita!’ Nayo wapita, ‘Majha!’ Nayo wakujha ni mbowa wanga, ‘Chita chindhu ichi! Nayo wachita.’ "

10 Yesu yapo wadavela chimwecho, wadazizwa, wadaakambila wandhu wajha adamchata, "Zene nikukambilani, sinidaone mundhu waliyonjhe mujhiko la Izilaeli uyo wali ni chikhulupi ngati ichi. 11 Zenedi nikukambilani, wandhu ambili siajhe kuchokela dela la kumwela ni kumpoto, nawo siakhale papwando pamojhi ni Ibulahimu ni Isaka ni Yakobo pa ufumu wa kumwamba. 12 Nambho wajha amafunika kukhala mu ufumu wa Mnungu saataidwe kubwalo mumdima, uko sikukhale chililo ni kukukuta mano." 13 Ndiipo Yesu wadamkambila yujha wamkulu wa Loma, "Pita kukhomo, ni ikhale ngati umo wakhulupilila."

Ni mbowa wake wadalama saa imweijha.

Yesu waalamicha wandhu ambili

14 Yesu wadafika kukhomo kwa Petulo, wadakomana apongozi wakazi Apetulo agona pachithanda, adwala matenda. 15 Yesu wadagafya jhanja la maye mmeneyo, ndhenda idamchoka, nayo wadanyakuka ni kuyamba kumuandalia chakudya.

16 Ujhulo yapo udafika, wandhu adampelekela Yesu wandhu ambili yawo adazamwa ni viwanda, Yesu wadavitopola viwanda, ni kwaalamicha odwala onjhe. 17 Wadachita chimwecho kuti yakwanile malembo ya mlosi Isaya, "Iye mwenewake watenga mavuto yathu, ni watenga matenda yathu."

Ochatila a Yesu umo afunika kukhala

18 Yesu yapo wadaliona gulu lalikulu la wandhu lamzungulila, wadalamula oyaluzidwa wake apite kuchijya la nyanja ya Galilaya. 19 Oyaluza thauko wadamsendelela, wadamkambila, "Oyaluza, sinikuchateni kwalikonjhe uko simpite."

20 Yesu wadayangha, "Nghandwe zali ni mbhanga, ni mbalami zali nivisa nambho mwana wa mundu walibe malo yo gona."

21 Mmojhi wa oyaluzidwa wake wadamkambila, "Ambuye, mniloleze uti nikaazike atate wanga."

22 Yesu wadamuyangha, "Nichate! Aleke wandhu yawo ali ngati amwalila azike wandhu yawo amwalila."

Yesu watuliza mwela

23 Yesu wadakwela mboti, ni oyaluzidwa wake adamchata. 24 Pampajha kudachokela mwela mnyanja, ata mafunde yadayamba kulibula boti. Yesu wadando gona litulo. 25 Oyaluzidwa adamchata, adamuucha nikukamba, "Ambuye, tilamicheni, titobila!"

26 Yesu wadaayangha, "Imwe wandhu achikulupi chochepa, ndandeyanji muopa?" Yesu wadaima nukutuliza mwela ni nyanja idagona.

27 Wandhu adadabwa, adajhifunjha, "Mundhu wabwanji uyu? Ata mbhepo ni mafunde vimvela!"

Yesu walamicha wandhu awili a viwanda

28 Yesu yapo wadafika kuchijha la nyanja mujhiko la Agadala, wadakomana ni wandhu awili yao amachoka kumainja, azamwa ni chiwanda. Wandhuwo adali owofya kupunda ni padalibe mundhu uyo wamapita mnjila imeneyo. 29 Pampajha adayamba kubula mapokoso, "Ufuna chiyani kwaife, iwe Mwana wa Mnungu? Bwanji, wajha kutivuticha ndhawi ikali yosakwanila?"

30 Pafupi ni malo yameyo padali nguluwe zambili zidali kudyela. 31 Ndiipo viwanda vidampembha Yesu, "Ngati utichocha tuloleze tikazilowe nguluwe zijha."

32 Yesu wadavikambila, "Haya pitani." Pamwepo lijha gulu la viwanda lidaachoka wandhu, lidalowa kwa nguluwe, ni gulu lonjhe la nguluwe lidachika pamchikililo nikufela mmajhi.

33 Wandhu owesa nguluwe wajha adathawa, adapita kumujhi. Kumeneko adakambilila nghani zijha zidaachokela wajha adazamwa ni viwanda. 34 Ndiipo, wandhu wonjhe adapita kukomana ni Yesu, adampembha kupunda wachoke mujhiko lao.

Veja também

Publicidade
Bíblia Online Bíblia Online

Bíblia Online • Versão: 2026-06-15_21-32-39-