Yesu wayesedwa
1 Ndiipo Mzimu Woyela udamchogoza Yesu mbaka kuphululu kuti waesedwe ni Satana. 2 Yesu wadamanga masiku alubaini usiku ni usana ndiipo wadavela njala. 3 Ndiipo woyesa wadamchata, Wadamkambila, "Ikakhala iwe Mwana wa Mnungu, Lamula myala iyi ikhale mabumunda."
4 Yesu wadamuyangha, "Yalembedwa, ‘Mundhu siwakhala wa moyo kwa bumundape, Nambho kwa kila malembo yoyela yakambidwa ni Mnungu.’"
5 Ndiipo Woyesa wadamtenga Yesu mbaka ku Yelusalemu mujhi woyela. Wadamkweza mbaka pamwamba kupunda pa chindupa la nyumba ya Mnungu. 6 Wadamkambila, "Ngati iwe ni Mwana wa Mnungu jhitaye panjhi. Pakuti yalembedwa,
‘Mnungu siwakutumile atumiki wake akumwamba
saakutenge mmanja mwao
kuti siudajhikhuwala mwendo wako pa mwala.’"
7 Yesu wadayangha, "Chinchijha yalembedwa, ‘Usadamuyesa Ambuye Mnungu wako.’"
8 Ndiipo Woyesa wadamtenganjho Yesu mbaka pa mwamba pa phili la litali. Wadamlangiza ufumu wonjhe wa jhiko ni ufulu wajhiko. 9 Wadamkambila, "Vindhu vonjhevi sinikupache ngati siunigwadile ni kunilambila."
10 Yesu wadamkambila, "Chokapo yapa iwe Woyesa! Yalembedwa mmalembo ya Mnungu, ‘Waalambile Ambuye Mnungu wako ni kwaatumikila iwo okha.’"
11 Ndiipo Woyesa wadamleka Yesu ni atumiki a kumwamba adajha kumtumikila.