45 Filipo yapo wadampheza Nasanaeli, wadamkambila, "Tampheza uyo Musa wadalemba nghani zake muchikalakala cha Thauko, ni uyo alosi adalemba nghani zake, ndekuti Yesu mwana wa Yusufu wa ku Nazaleti."
46 Nasanaeli nayonjho wadamfunjha Filipo, "Bwanji, chindhu cha bwino chikhoza kuchokela ku Nazaleti?"
Ndiipo Filipo wadayangha, "Majha uone."