Yesu walowa ku Yelusalemu kokondwa
12 Mawa lake gulu lalikulu la wandhu anyiyao adajha ku pwando la Pasaka, adavela kuti Yesu wali mnjila kujha ku Yelusalemu. 13 Ndiipo adatenga ndhawi za zing’onozing’ono za mitengo ya mitende, ni kupita kumlandila, adakweza mvekelo ni kukamba, "Uelekelo! Wapachidwe mwawi uyo wakujha kwa jhina la Ambuye. Wapachidwe mwawi Mfumu wa Izilaeli!"