Pular para o conteúdo
Publicidade

Yohana 12

Yesu walowa ku Yelusalemu kokondwa

12 Mawa lake gulu lalikulu la wandhu anyiyao adajha ku pwando la Pasaka, adavela kuti Yesu wali mnjila kujha ku Yelusalemu. 13 Ndiipo adatenga ndhawi za zing’onozingono za mitengo ya mitende, ni kupita kumlandila, adakweza mvekelo ni kukamba, "Uelekelo! Wapachidwe mwawi uyo wakujha kwa jhina la Ambuye. Wapachidwe mwawi Mfumu wa Izilaeli!"

Veja também