Pular para o conteúdo
Publicidade

João 14

21 "Uyo wayalandila malamulo yanga ni kuyagwila, mmeneyo nde uyo wanikonda. Uyo wanikonda ine siwakondedwe ni Atate wanga, nane sinimkonde ni kujhijhiwicha kwa iye."

22 Chimwecho Yuda nambho osati Isikaliyote adamkambila, "Ambuye, sikhozeke bwanji mujhilangize kwa ife ni osati kwa jhiko?"

23 Yesu wadayangha, "Wandhu yao anikonda akalichitila njhito mawu langa ni Atate wanga saakonde, nafe sitijhe kwa anyiiwo ni kukhala pamojhi nawo. 24 Uyo siwanikonda siwayachitila njhito mawu yanga. Uthenga uwo muuvela osati wanga nambho uchokela kwa Atate yao anituma."

Veja também