9 Yesu wadamkambila, "Filipo nakhala namwe ndhawi yonjheyi, ukali osanijhiwe? Uyo waniona ine waona Atate. Ukamba bwanji, ‘Tilangizeni Atate?’ 10 Bwanji, siukhulupilila kuti ine nili mkati mwa Atate, ni Atate ali mkati mwanga? Mawu yayo nikukambilani osati kwa lamulo langa, Atate yawo alimkati mwanga achita njhito zao.