Pular para o conteúdo
Publicidade

Yohana 15

Yesu Mzabibu wa Uzene

1 Ndiipo Yesu wadakamba, "Ine ni mzabibu wa zene, ni Atate nde amlimi. 2 Ndhawi yaliyonjhe iyo siibala vipacho mkati mwanga, Atate aidula, ni ndhawi iyo ibala aikonjezela ijhipunda kubala. 3 Anyiimwe mwatho elechedwa muuzimu ndande ya uthenga uwo nidakuyaluzani. 4 Khalani mkati mwanga, ngati umo ine nikhalila mkati mwanu. Ngati umo ndhawi ya mzabibibu siikhoza kubala yokha vipacho popande kukhala mumtengo wa mzabibu, chimwecho anyiimwe simukhoza kuchita chijha achifuna Amnungu ngati simukhala mkati mwanga."

5 "Ine ni mzabibu, anyiimwe ni ndhawi. Yao akhala mkati mwanga, nane nikakhala mkati mwao, achameneo sachite vindhu vabwino vambili, popande ine simukhoza kuchita kandhu.

Veja também