Pular para o conteúdo
Publicidade

Yohana 19

25 Pafupi ni mtanda wa Yesu adaima amaye wake, akulu wao wa amake, Malia wamkazi wa Kileopa, ni Malia uyo wadachokela kumujhi wa Magidala. 26 Yesu yapo wadaona amake aima pafupi ni oyaluzidwa uyo wamamkonda, wadaakambila amaye wake, "Maye! Mwana wanu uyo yapo."

27 Ndiipo wadamkambila yujha oyaluzidwa wake Yohana, "Amaye wako yawo yapo." Kuyambila ndhawi imeneyo oyaluzidwayo wadatengedwa ni amaye wake Ayesu kukhala kukhomo kwao.

Veja também