Pular para o conteúdo
Publicidade

João 9

Yesu wamlamicha mundhu uyo wabadwa osapenya

1 Siku limojhi Yesu yapo wamapita wadamuona mundhu mmojhi, uyo siwapenya kuyambila kubadwa kwake. 2 Basi oyaluzidwa wake adamfunjha, "Oyaluza! Yani wachita machimo, mundhu uyu kapina obala wake, mbaka wabadwe osapenye?"

3 Yesu wadaayangha, "Wabadwa osapenye osati ndande ya machimo yake, kapina ya obala wake, wadabadwa chimwecho kuti mbhavu ya Amnungu iwoneke muumoyo wake. 4 Ifunika tiendekele kuzichita njhito za yawo atituma kukali usana, ndande usiku ukujha uwo mundhu waliyonjhe siwakhoza kuchita njhito. 5 Ndhawi nili pano pajhiko, ine nde dangalila la wandhu a pajhiko."

6 Yapo wadakamba chimwecho, wadalavula malovu panjhi, wadakonja thokope, wadamnyeka yujha osapenyeyo mmaso, 7 wadamkambila, "Pita ukasambe kuthiwi la Siloamu." Mawu Siloamu mate yake Uyo watumidwa. Chimwecho wadapita kusamba, wadabwela uku ni wapenya.

Veja também