Pular para o conteúdo
Publicidade

Lucas 7

31 Yesu wadayendekela kukamba, "Bwanji, sinalinganiche ni chiani, wandhu a mbadwa uno? Bwanji, wandhu anyiyawa ni amtundu wanji? 32 Ali ngati wana wokhala pamalo yayo amakomanilana wandhu, naatanana achinawene kwa achinawene wake,

Takutimbilani vitolilo, nambho simudavine!

Takuyimbilani nyimbo za zaya nambho simudalile!

33 Pakuti Yohana mbatizi yapo wadafika, niwamanga kudya ni wosamwe divayi kila ndhawi, ni anyiimwe mudamnena kuti, Wali ni viwanda!34 Nayenjho mwana wa Mundhu wafika, wakudya ni wakumwa, namwe mkambanjho, Muoneni uyu! Waludyo ni wolojhela, bwenji wa wolandila malipilo ni wochimwa!35 Nambho, ekima ya Mnungu yavomelezewa kuti ni yabwino kwa wonjhe yawo ayivomela."

Yesu wanyekedwa mafuta ni wamkazi wochimwa

36 Siku limojhi, mfalisayo mmojhi wadamlalika Yesu kujha kudya chakudya cha ujhulo cha mnyumba mwake. Yesu nayonjho wadalowa mnyumba mwa mfalisayo yujha, wadakhala pa chitembwe ni kudya chakudya. 37 Ndiipo, mmujhi ujha mudali wamkazi mmojhi uyo wadali wochimwa. Yapo wadavela kuti Yesu watokudya mnyumba ya mfalisayo, wadatenga njhupa iyo lidajhala mafuta yonunghila.

Veja também