Pular para o conteúdo
Publicidade

Mateus 1

20 Yusufu yapo wamaganizila chindhu ichi, Mtumiki wa kumwamba wa Ambuye wadamjhela kumaloto kumkambila Yusufu mwana wa Daudi, Usadaopa kumtenga Maliya kukhala mkazako pakuti pathupi pake pajha kwa mbhavu za Mzimu Woyela. 21 Nayo siwabale mwana wa mmuna. Nawe siumtane jhina lake Yesu pakuti uyu nde uyo siwaombole wandhu wake kuchoka ku machimo yao.

Veja também