20 Yesu wadaayangha, "Ndande ya chikhulupi chanu chochepa. Nikukambilani uzene, ngati mdakakhala ni chikulupi ngati mbeu ya aladali, mdakakhoza kulikambila phili ili, ‘Chokapo upite yapo’ nalo udakapita. Palibe chindhu icho sichilepeleke kwanu. 21 Chiwanda cha mtundu uwu sichikhoza kuchochedwa kwa njila iliyonjhe, nambho kwa kumanga ni kupemdhela."