16 Pampajha, Yesu yapo wadamaliza kubatizidwa wadachuuka mmajhi. Kumwamba kudamasuka ni wadaona Mzimu wa Mnungu niuchika ngati nghunda ni kutula pamwamba pake. 17 Mwachizulumukila mvekelo kuchokela kumwamba udaveka, "Uyu nde Mwana wanga wokondedwa uyo nikondwela nayo."
Publicidade