11 Chipano nikujha kwanu, sinilinjho mujhiko, nambho anyiiwo alimujhiko. Atate awokha! Kwa ulamulilo wanu uwo mwanipacha, pepani mwasunge ochatila wanga akhale ni umojhi ngati umo ife tili amojhi. 12 Yapo nidali nao, nidaasunga k mudanipacha. Ine nidaasunga, palibe uyo wadasowa, nambho mwana uyo wadafunika kuyomwa, dala malembo yakwanile.