Pular para o conteúdo
Publicidade

João 21

Yesu wampacha maagizo Petulo

15 Yapo adadya, Yesu wadamfunjha Simoni Petulo, "Simoni Petulo mwana wa Yohana! Bwanji, unikonda ine kupitilila anyiyawa?"

Nayo wadayangha, "Etu, Ambuye, mujhiwa nikukondani."

Yesu wadamkambila, "Dyecha gulu la mbelele zanga." 16 Ndiipo Yesu wadamfujhanjho kakawili, "Simoni mwana wa Yohana! Bwanji, unikonda?"

Petulo wadayangha, "Etu, Ambuye, mujhiwa nikukondani."

Yesu wadamkambila, "Sunga mbelele zanga." 17 Wadamfunjha kakatatu, "Simoni mwana wa Yohana! Bwanji, unikonda?"

Petulo wadadandaula kupunda ndande wadamfunjha katatu, "Unikonda?" Wadamkambila, "Ambuye, imwe mujhiwa yonjhe, mujhiwa kuti nikukondani."

Yesu wadamkambila, "Dyecha gulu la mbelele zanga.

Veja também