Pular para o conteúdo
Publicidade

João 6

19 Oyaluzidwa yapo adapita patali ngati meta zitatu kapina zinai, adamuona Yesu ni waenda pamwamba pa majhi, wadawandikila sitima, adaopa kupunda. 20 Ndiipo Yesu wadakambila, "Simudaopa, ni ine!" 21 Yapo adamkalibisha Yesu mu mbwato, ndhawi imweyo adafika kujhiko ilo amapita.

Veja também