Pular para o conteúdo
Publicidade

João 6

44 Palibe mundhu uyo wakhoza kujha kwanga, ngati siwadaghuzidwe ni Atate yao anituma, nane sinimuhyuche mundhu mneyo siku lo thela. 45 Yalembedwa mvikalakala va alosi, Wandhu wonjhe sayaluzidwe ni Amnungu.Waliyonjhe uyo waavela Atate ni kujhiyaluza kwa iwo, wakujha kwanga. 46 Palibe uyo waonapo Atate, nambho uyo wachoka kwa Amnungu, mmeyo nde uyo waona Atate. 47 Nikukambilani zene, uyo wakhulupilila wali ni umoyo wa muyaya.

Veja também