Pular para o conteúdo
Publicidade

Luka 10

39 Masa wadali ni mwali mnjake uyo wamatanidwa Maliya, mmeneyo wadakhala pafupi ni mmiyendo mwa Yesu kuvechela mayaluzo yake. 40 Nambho Masa wamachauchika ni njhito zambili. Ndiipo wadamchata Yesu ni kumkambila, "Ambuye, bwanji simuona kuti mbale wanga wanisiila nichite njhito zonjhe nekha? Mkambileni wakanithangatile."

Estes versículos te tocaram? Ore agora!

+581 estão orando agora.

Junte-se à corrente de oração.

Veja também