2 Yesu wadakambila, "Yapo mupembhela, kambani chimwechi,
‘Atate wathu akumwamba!
Jhina lanu lilemekezedwe kuti ni Loyela,
ufumu wanu ujhe.
3 Mutipache chakudya chathu cha siku ni siku.
4 Mutilekelele volakwa vathu,
ngati umo ife talekelela yawo atilakwila,
musaditipeleka mmayeselo.’ "