Publicidade

Lucas 12

Uyo wafunika kuopedwa

4 "Nikukambilani anyiimwe achabwenji langa, msadawaopa anyiyawo akupha thupi, anyiyawo pambuyo pa yameneyo saakhoza kuchita chilichonjhe. 5 Nambho, sinikulangizeni uyo mufunika kumuopa, muopeni yujha pambuyo pakupha thupi wakhoza kukuponyani kumoto wosathima muyaya. Zenedi nikukambilani, muopeni iye.

Veja também

Bíblia Online Bíblia Online

Bíblia Online • Versão: 2026-07-05_19-25-13-