Pular para o conteúdo
Publicidade

Luka 19

37 Yapo wadawandikila ku Yelusalemu, pa njila iyo ichikila pa phili la mizeituni, gulu lonjhe la wochatila wake adayamba kukondwela ni kumtamanda Mnungu pokweza mvekelo ndande ya vodabwicha vonjhe ivo adavionapo. 38 Adakamba, "Wali ni mwawi Mfumu uyo wakujha mu jhina la Ambuye. Mtendele ukhale kumwamba kwa Mnungu, ni ulemelelo kumeneko kumwamba kupunda!"

Veja também