Pular para o conteúdo
Publicidade

Luka 2

Yesu wapita panyumba ya Mnungu

41 Yusufu ni Maliya adali ni chikalidwe chopita ku Yelusalemu kila chaka ndhawi ya phwando la Pasaka. 42 Yapo Yesu wadafika msinghu wa vyaka khumi ni viwili, wadapita pamojhi ni wobala wake kuphwando ngati umo chidali chikalidwe chao. 43 Yapo lidatha phwando lijha, wobala wake adayamba ulendo wobwelela kupita ku Yelusalemu, nambho Yesu wadakhalila ku Yelusalemu popande kujhiwa wobala wake. 44 Anyaiwo amaganiza kuti wali pamojhi ni gulu la ulendo, chimwecho adayenda siku lambhumbhu. Ndiipo adayamba kumfunafuna pakati pa abale ni abwenji. 45 Yapo adalepela kumuona, adabwelela ku Yelusalemu kumfunafuna.

46 Pambuyo pa masiku yatatu adamuona panyumba ya Mnungu, wakhala pakatikati pa oyaluza thauko, niwavechela ni kwaafunjha mafunjho. 47 Wandhu wonjhe adavela mayaluzo yake adazizwa kujhiwa kwake ni umo wamayanghila kwa hekima. 48 Wobala wake yapo adamuona adazizwa kupunda. Maliya, make wamwanayo wadamfunjha, "Mwana wanga, ndande yanji watichitila chimwechi? Atate wako ni ine timakufunafuna tali ni mandha." 49 Iye wadaafunjha, "Ndande yanji mnifunafuna ine? Bwanji, simujhiwa kuti ine nifunika kukhalapo panyumba ya atate wanga?" 50 Nambho wobala wake siadajhiwe mate ya mawu yayo wadakambila mwana wao.

51 Ndiipo Yesu wadabwela pamojhi ni anyiiwo mbaka ku Nazaleti, iye wamavela. Nambho amake adavisunga vindhu vonjhe mumtima. 52 Nayo Yesu wadaendekela kukula msinghu ni hekima, wadayendekela kumkhadwilicha Mnungu ni wandhu.

Veja também