6 Yapo adali kumeneko ku Beselehemu, ndhawi yojhipenyelela Maliya idakwanila, 7 ni wadajhimasula mwana wake wachisamba, wammuna. Iye wadamvinikila matewela ni kumgoneka mchidiku chasependwa ndande yodyechela ng’ombe, chifuko anyiiwo siadapate malo mnyumba ya alendo.
Publicidade
Publicidade