Pular para o conteúdo
Publicidade

Luka 8

Wachikazi yawo adachogozana ni Yesu

1 Pambuyo pa yaya Yesu wadapita kumijhi ni ku vijhijhi kulalikila Uthenga Wabwino wa Ufumu wa Mnungu. Ni woyaluzidwa wake khumi ni awili wadachogozana naye. 2 Ni wachikazi wina adachochedwa viwanda, ni kwalamicha matenda yawo, adapiata pamojhi ni iye. Wachikaziwo adali, Maliya kuchokela ku Magedelena, uyo wadachochedwa viwanda saba, 3 Ni Yoane mkazake wa Kuza, wamkulu wa alonda wa nyumba ya Helode, Susana ni wina ambili. Wachikazi anyiyawa amamthangatila Yesu pamojhi ni oyaluzidwa wake kwa chuma chao achinawenewake.

Veja também