Pular para o conteúdo
Publicidade

Matayo 2

Alendo kuchokela ku dela la kumwela

1 Yesu wadabadwa ku mujhi wa Beselehemu mjhiko la Yudea. Ndhawi imeneyo Helode wadali mfumu. Yesu yapo wadandobadwa wandhu yawo amajhiwa icho sichichokele adafika ku Yelusalemu 2 adaafunjha, "Walikuti mwana uyo wabadwa Mfumu wa Ayahudi? Pakuti tayiona ndhondwa yake kudela la kumwela ni nafenjho tajha kumulambila."

3 Mfumu Helode ni wandhu wonjhe yawo adali ku Yelusalemu yapo adavela nghani zimenezo wadavutika mumtima. 4 Mfumu Helode wadaatana pamojhi waakulu ajhukulu ni woyaluza mathauko wadaafunjha, "Kilisito wabadwila kuti?"

5 Adamuyangha, "Wabadwila mmujhi wa Beselehemu mjhiko la Yudea pakuti nde umo wadalembela mlosi,

6 Iwe Beselehemu mujhi wa Yudea,

mujhi wanu ni waukulu pakati pa mijhi yojhiwika mu Yudea.

Pakuti kwanu siwachokele mchogoleli,

uyo siwaachogoze wandhu wanga Izilaeli."

7 Helode wadaatana kwa chisisi wandhu wajha ajhiwa yayo siyachokele kwa kupenya ndhondwa ni kwaafunjha ndhawi iyo idaonekana ndhondwa. 8 Wadaatuma ku Beselehemu ni kwaakambila, "Mapitani mkafunjhile bwino nghani za mwanayo. Yapo simumuone mbwele munikambile kuti nanenjho nipite nikamulambile."

9 Yapo adamaliza kumvechela mfumu adachoka ni ndhondwa iyo adaiwona kuchoka kudela la kumwela idaachogoza ni kuima pajha wadali mwana. 10 Yapo adaiona ndhondwa ijha adakondwa kupunda. 11 Ndiipo adalowa mnyumba ni adamuona mwana pamojhi ni Maliya maye wake. Adagwada ni kumlambila. Adamasula mbhaso zao ni kumpacha mwana zaabu ni ubani ni mnghwala uwo utanidwa manemane.

12 Ndiipo Mnungu adaonya kumaloto kuti asadabwelela kwa Helode. Chimwecho adabwela kujhiko lawo kwa kupitila njila yina.

Veja também