28 Adamvula njhalu zake ni kumveka njhalu ya chifumu. 29 Adasoka nghata ya minga nikumveka kumutu, adamwikila mkwapulo kujanja lake la kwene. Adagwada pachogolo pake ni kumchitila vipongwe uku niakamba, "Moni mfumu wa Ayahudi!"
Publicidade
Publicidade