Pular para o conteúdo
Publicidade

Lucas 1

Kubadwa kwa Yesu kuuzilidwa

26 Mumwezi wa sita wa pathupi pa Elizabeti, Mnungu wadamtuma mtumiki wake Gabilieli kupita kumujhi wa Galilaya, uwo utanidwa Nazaleti, 27 wapite kwa mwalimbeta uyo wamatanidwa Maliya, uyo wadapachidwa chilipa ni wammuna uyo wamatanidwa Yusufu, wa mbadwa wa Daudi. 28 Mtumiki wa kumwamba wa Mnungu wadamchokela ni kumlonjela ni kumkambila, "Iwe wapachidwa mwawi, Ambuye ali pamojhi ni iwe!" 29 Maliya yapo wadavela moni imeneyo wadaiganizila kupunda niwadakamba kuti moni iyi mate yake chiyani. 30 Nambho mtumiki wa kumwamba wa Mnungu wadamkambila, "Maliya usadaopa, pakuti Mnungu wakupacha mwawi. 31 Vechela, siupate pathupi ni kubala mwana wa mmuna, niiwe siumpache jhina Yesu. 32 Iye siwakhale mundhu waulamulilo, ni siwatanidwe mwana wa Uyo wali kumwamba kupunda. Ni Ambuye Mnungu sampache ufumu ngati umo wadali Daudi, tate wake. 33 Chimwecho iye siwalamulile mbadwa wa Yakobo muyaya, ni ufumu wake siukhala ni mathelo!" 34 Maliya wadamuyangha ni kumfunjha mtumiki wa kumwamba wa Mnungu, "Sivikhozekane bwanji vindhu ivi, pakuti sinidapezane chithupi ni wammuna?" 35 Mtumiki wa kumwamba wa Mnungu wadamuyangha Maliya, "Mzimu woyela siukujhele iwe, ni mphavu zake uyo wali kumwamba kupunda sizikuvinikile iwe ngati chitunjhi. Chimwecho, ni Woyela uyo siwabadwe siwatanidwe Mwana wa Mnungu. 36 Ata mbale wako Elizabeti uyo wamatanidwa wambende, chipano wali ni pathupi pa miyezi sita, ingakhale iye ni mzee kupunda. 37 Mate yake palibe chindhu icho sichikhozeka kwa Mnungu." 38 Maliya wadayangha, "Ine ni mbowa wa Ambuye, mawu yaya yachitike ngati umo mwakambila." Ndiipo mtumiki wa kumwamba wadachokapo.

Veja também